Yeremiya 28:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Yeremiya mneneri anati kwa Hananiya mneneri pamaso pa ansembe, ndi pamaso pa anthu onse amene anaima m'nyumba ya Yehova, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Yeremiya mneneri anati kwa Hananiya mneneri pamaso pa ansembe, ndi pamaso pa anthu onse amene anaima m'nyumba ya Yehova, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Apo mneneri Yeremiya adayankha mneneri Hananiya pamaso pa ansembe ndi anthu onse amene anali m'Nyumba ya Chauta. Adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pamenepo mneneri Yeremiya anayankha mneneri Hananiya pamaso pa ansembe ndi anthu onse amene anasonkhana mʼNyumba ya Yehova. Onani mutuwo |