Yeremiya 28:13 - Buku Lopatulika13 Pita, nunene kwa Hananiya, kuti Yehova atero: Wathyola magoli amtengo; koma udzapanga m'malo mwao magoli achitsulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pita, nunene kwa Hananiya, kuti Yehova atero: Wathyola magoli amtengo; koma udzapanga m'malo mwao magoli achitsulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Pita ukamuuze Hananiya mau a Chauta akuti, ‘Iweyo wathyola goli lamtengo, m'malo mwake Ine ndidzaika goli lachitsulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 “Pita, kawuze mneneri Hananiya kuti, ‘Yehova akuti: Iwe wathyola goli lamtengo, mʼmalo mwake Ine ndidzayika goli lachitsulo. Onani mutuwo |