Yeremiya 27:19 - Buku Lopatulika19 Pakuti Yehova wa makamu atero, za zoimiritsa, ndi za thawale, ndi za zoikirapo, ndi za zipangizo zotsala m'mzinda uwu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Pakuti Yehova wa makamu atero, za zoimiritsa, ndi za thawale, ndi za zoikirapo, ndi za zipangizo zotsala m'mudzi uwu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Chauta Wamphamvuzonse ndiye akunena za mizati, chimbiya, maphaka ndi ziŵiya zonse zimene zidatsala mumzindamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Pakuti Yehova akunena za zipilala, za mbiya ya madzi, maphaka ndi ziwiya zina zimene zatsala mu Yerusalemu. Onani mutuwo |