Yeremiya 27:14 - Buku Lopatulika14 Musamvere mau a aneneri amene anena ndi inu, kuti, simudzamtumikira mfumu ya ku Babiloni; pakuti akunenerani zonama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Musamvere mau a aneneri amene anena ndi inu, kuti, simudzamtumikira mfumu ya ku Babiloni; pakuti akunenerani zonama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Musaŵamvere aneneri okuuzani kuti musadzatumikire mfumu ya ku Babiloni. Akukuloserani zabodza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Musamvere mawu a aneneri akamakuwuzani kuti, ‘Simudzatumikira mfumu ya ku Babuloni,’ chifukwa zimene akukuloseranizo nʼzabodza. Onani mutuwo |