Yeremiya 26:22 - Buku Lopatulika22 ndipo Yehoyakimu mfumu anatuma anthu ku Ejipito, Elinatani mwana wake wa Akibori, ndi anthu ena pamodzi ndi iye, anke ku Ejipito; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 ndipo Yehoyakimu mfumu anatuma anthu ku Ejipito, Elinatani mwana wake wa Akibori, ndi anthu ena pamodzi ndi iye, anke ku Ejipito; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Komabe mfumu Yehoyakimu adatuma Elinatani mwana wa Akibori, pamodzi ndi anthu ena, ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Komabe Mfumu Yehoyakimu anatuma Elinatani mwana wa Akibori pamodzi ndi anthu ena, ku Igupto. Onani mutuwo |