Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 26:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo anauka akulu ena a m'dziko, nati kwa msonkhano wa anthu, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo anauka akulu ena a m'dziko, nati kwa msonkhano wa anthu, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Akuluakulu ena am'dzikomo adaimiriranso nauza anthu onse amene adasonkhanawo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Akuluakulu ena a mʼdzikomo anayimirira ndi kuwuza gulu lonse la anthu kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 26:17
3 Mawu Ofanana  

Mika Mmoreseti ananenera masiku a Hezekiya mfumu ya Yuda; ndipo iye ananena kwa anthu onse a Yuda, kuti, Yehova wa makamu atero: Ziyoni adzalimidwa ngati munda, Yerusalemu adzakhala miunda, ndi phiri la nyumba longa misanje ya nkhalango.


Mau a Yehova amene anadza kwa Mika wa ku Moreseti masiku a Yotamu, Ahazi, ndi Hezekiya, mafumu a Yuda, amene adaona za Samariya ndi Yerusalemu.


Koma ananyamukapo wina pabwalo la akulu a milandu, ndiye Mfarisi, dzina lake Gamaliele, mphunzitsi wa malamulo, wochitidwa ulemu ndi anthu onse, nalamula kuti atumwiwo akhale kunja pang'ono.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa