Yeremiya 26:16 - Buku Lopatulika16 Pamenepo akulu ndi anthu onse anati kwa ansembe ndi kwa aneneri, Munthu uyu sayenera kufa: pakuti watinenera ife m'dzina la Yehova Mulungu wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamenepo akulu ndi anthu onse anati kwa ansembe ndi kwa aneneri, Munthu uyu sayenera kufa: pakuti watinenera ife m'dzina la Yehova Mulungu wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pamenepo akuluakuluwo ndi anthu ena adauza ansembe ndi aneneri kuti, “Munthuyu sayenera kufa, popeza kuti walankhula nafe m'dzina la Chauta, Mulungu wathu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pamenepo ndunazo pamodzi ndi anthu onse anawuza ansembe ndi aneneri kuti, “Munthu uyu sayenera kuphedwa! Pakuti wayankhula kwa ife mʼdzina la Yehova Mulungu wathu.” Onani mutuwo |