Yeremiya 26:14 - Buku Lopatulika14 Koma ine, taonani, ndili m'manja anu; mundichitire ine monga mokomera ndi moyenera m'maso anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma ine, taonani, ndili m'manja anu; mundichitire ine monga mokomera ndi moyenera m'maso anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ineyo ndili m'manja mwanu. Mundichite chilichonse chimene chikukomereni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kunena za ine, ndili mʼmanja mwanu; mundichite chilichonse chimene mukuganiza kuti ndi chabwino ndi choyenera. Onani mutuwo |