Yeremiya 25:2 - Buku Lopatulika2 amene mneneri Yeremiya ananena kwa anthu onse a Yuda, ndi onse okhala mu Yerusalemu, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 amene mneneri Yeremiya ananena kwa anthu onse a Yuda, ndi onse okhala m'Yerusalemu, kuti: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mneneri Yeremiya adauza anthu onse a ku Yuda ndi onse okhala ku Yerusalemu kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Choncho mneneri Yeremiya anawuza anthu onse a ku Yuda pamodzi ndi onse amene amakhala mu Yerusalemu kuti: Onani mutuwo |