Yeremiya 24:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ndidzatuma lupanga, ndi njala, ndi mliri mwa iwo, mpaka athedwa m'dziko limene ndinapatsa iwo ndi makolo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ndidzatuma lupanga, ndi njala, ndi chaola mwa iwo, mpaka athedwa m'dziko limene ndinapatsa iwo ndi makolo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndidzaŵapha ndi nkhondo, njala ndi mliri, mpaka onsewo nditaŵapululiratu m'dziko limene ndidaŵapatsa iwowo ndi makolo ao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndidzawatumizira nkhondo, njala ndi mliri mpaka atawonongedwa mʼdziko limene ndinawapatsa iwo ndi makolo awo.’ ” Onani mutuwo |