Yeremiya 23:12 - Buku Lopatulika12 Chifukwa chake njira yao idzakhala kwa iwo yonga malo akuterereka m'mdima; adzachotsedwa, nadzagwa momwemo; pakuti ndidzawatengera zoipa, chaka cha kulangidwa kwao, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Chifukwa chake njira yao idzakhala kwa iwo yonga malo akuterereka m'mdima; adzachotsedwa, nadzagwa momwemo; pakuti ndidzawatengera zoipa, chaka cha kulangidwa kwao, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Nchifukwa chake njira zao zidzakhala zoterera. Adzaŵapirikitsira kumdima kumene akagwe. Ndidzaŵaonetsa ndoza pa nthaŵi ya chilango chao,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Nʼchifukwa chake njira zawo zidzakhala zoterera; adzawapirikitsira ku mdima ndipo adzagwera kumeneko. Adzaona zosaona mʼnthawi ya chilango chawo,” akutero Yehova. Onani mutuwo |