Yeremiya 23:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti mneneri ndi wansembe onse awiri adetsedwa; inde, m'nyumba yanga ndapeza zoipa zao, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti mneneri ndi wansembe onse awiri adetsedwa; inde, m'nyumba yanga ndapeza zoipa zao, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Zoonadi, aneneri ndiponso ansembe, onsewo saopa Mulungu. Ndaŵapeza akuchita zoipa ngakhale m'Nyumba mwanga,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Mneneri ngakhale wansembe onse sapembedza Yehova. Amachita zoyipa ngakhale mʼnyumba yanga,” akutero Yehova. Onani mutuwo |