Yeremiya 23:1 - Buku Lopatulika1 Tsoka abusa amene athetsa nabalalitsa nkhosa za busa langa! Ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Tsoka abusa amene athetsa nabalalitsa nkhosa za busa langa! Ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Tsoka kwa abusa amene amaononga ndi kumwaza nkhosa za pabusa panga,” akutero Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Tsoka kwa abusa amene akuwononga ndi kubalalitsa nkhosa za pabusa panga!” akutero Yehova. Onani mutuwo |