Yeremiya 22:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti Yehova atero za nyumba ya mfumu ya Yuda: Ndikuyesa iwe Giliyadi, ndi mutu wa Lebanoni; koma ndidzakuyesa iwe chipululu, ndi mizinda yosakhalamo anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti Yehova atero za nyumba ya mfumu ya Yuda: Ndikuyesa iwe Giliyadi, ndi mutu wa Lebanoni; koma ndidzakuyesa iwe chipululu, ndi midzi yosakhalamo anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Naŵa mau a Chauta onena za nyumba ya mfumu ya ku Yuda: “Ngakhale iwe ndimakukonda ngati Giliyadi, kapena ngati nsonga ya phiri la Lebanoni, komabe ndidzakusandutsa chipululu, mzinda wopanda anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakuti zimene Yehova akunena za nyumba yaufumu ya mfumu ya ku Yuda ndi izi: “Ngakhale iwe uli ngati Giliyadi kwa Ine, ngati msonga ya phiri la Lebanoni, komabe ndidzakusandutsa chipululu, ngati mizinda yopanda anthu. Onani mutuwo |