Yeremiya 22:5 - Buku Lopatulika5 Koma ngati simudzamva mau amenewa, Ine ndilumbira, pali Ine mwini, ati Yehova, nyumba iyi idzakhala yabwinja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma ngati simudzamva mau amenewa, Ine ndilumbira, pali Ine mwini, ati Yehova, nyumba iyi idzakhala yabwinja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma ngati sudzamvera mau anga, ndikulumbira pali Ine ndemwe, kuti nyumba imeneyi idzasanduka bwinja!’ ” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma ngati sumvera malamulo awa, akutero Yehova, ndikulumbira pali Ine ndemwe kuti nyumba ino yaufumu idzasanduka bwinja.’ ” Onani mutuwo |