Yeremiya 22:30 - Buku Lopatulika30 Atero Yehova, Lembani munthu uyu wopanda ana, munthu wosaona phindu masiku ake; pakuti palibe munthu wa mbeu zake adzaona phindu, ndi kukhala pa mpando wachifumu wa Davide, ndi kulamuliranso mu Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Atero Yehova, Lembani munthu uyu wopanda ana, munthu wosaona phindu masiku ake; pakuti palibe munthu wa mbeu zake adzaona phindu, ndi kukhala pa mpando wachifumu wa Davide, ndi kulamuliranso m'Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Chauta akuti, “Munthu ameneyu mumtenge ngati wopanda ana, munthu amene sadzakhoza pa moyo wake. Ndithu, palibe ndi mmodzi yemwe mwa zidzukulu zake amene adzakhale pa mpando waufumu wa Davide ndi kudzalamuliranso Yuda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Yehova akuti, “Munthu ameneyu mumutenge ngati wopanda ana, munthu amene sadzakhala wochita bwino pamoyo wake wonse, pakuti palibe ndi mmodzi yemwe mwa zidzukulu zake zomwe zidzachita bwino. Palibe amene adzathe kukhala pa mpando waufumu wa Davide ndi kulamulira Yuda.” Onani mutuwo |