Yeremiya 22:23 - Buku Lopatulika23 Iwe wokhala mu Lebanoni, womanga chisa chako m'mikungudza, udzachitidwa chisoni chachikulu nanga pamene mapweteko adzadza kwa iwe, monga mkazi alinkudwala! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Iwe wokhala m'Lebanoni, womanga chisa chako m'mikungudza, udzachitidwa chisoni chachikulu nanga pamene mapweteko adzadza kwa iwe, monga mkazi alinkudwala! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Inu amene mumakhala ku nyumba ya ku Lebanoni ija, amene mudamanga nyumba zanu pakati pa mikungudza, mudzalira kwambiri pamene zoŵaŵa zidzakugwerani, zonga za mkazi pa nthaŵi yake yochira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Inu amene mumakhala mʼnyumba ya ku Lebanoni, amene munamanga nyumba zanu pakati pa mikungudza, mudzabuwula kwambiri pamene zowawa zidzakugwerani, zonga za mkazi pa nthawi yake yochira! Onani mutuwo |