Yeremiya 22:19 - Buku Lopatulika19 Adzamuika monga kuika bulu, adzamkoka nadzamponya kunja kwa zipata za Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Adzamuika monga kuika bulu, adzamkoka nadzamponya kunja kwa zipata za Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Adzamuika ngati bulu basi, kuchita kumguguza nkukamtaya kuseri kwa zipata za Yerusalemu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Adzayikidwa ngati bulu, kuchita kumuguguza ndi kukamutaya kunja kwa zipata za Yerusalemu.” Onani mutuwo |