Yeremiya 22:18 - Buku Lopatulika18 Chifukwa chake Yehova atero za Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda: Sadzamlira iye, kuti, Kalanga ine mbale wanga! Kapena, Kalanga ine mlongo wanga! Sadzamlira, kuti, Kalanga ine mbuye! Kapena, Kalanga ine ulemerero wake! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Chifukwa chake Yehova atero za Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda: Sadzamlira iye, kuti, Kalanga ine mbale wanga! Kapena, Kalanga ine mlongo wanga! Sadzamlira, kuti, Kalanga ine mbuye! Kapena, Kalanga ine ulemerero wake! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Nchifukwa chake Chauta ponena za Yehoyakimu mwana wa Yosiya, mfumu ya ku Yuda, akuti, “Sipadzakhala womulira munthu ameneyo kuti, ‘Kalanga ine, mbale wanga!’ Kapena kuti, ‘Kalanga ine, mlongo wanga!’ Sipadzakhala womulira kuti, ‘Kalanga ine, mbuye wanga!’ Kapena kuti, ‘Kalanga ine, mfumu yanga.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Nʼchifukwa chake Yehova ponena za Yehoyakimu mwana wa Yosiya mfumu ya ku Yuda akuti, “Anthu sadzamulira maliro kapena kunena kuti, ‘Kalanga ine, mʼbale wanga! Kalanga ine mlongo wanga! Anthu ake sadzamulira maliro kuti, Kalanga ine, mbuye wathu! Taonani ulemerero wake wapita!’ Onani mutuwo |