Yeremiya 22:16 - Buku Lopatulika16 Iye anaweruza mlandu wa aumphawi ndi osowa; kumeneko kunali kwabwino. Kodi kumeneko si kundidziwa Ine? Ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Iye anaweruza mlandu wa aumphawi ndi osowa; kumeneko kunali kwabwino. Kodi kumeneko si kundidziwa Ine? Ati Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ankateteza anthu otsika ndi osauka, ndipo zonse zinkamuyendera bwino. Kodi zimenezi sizidaonetse kuti ankandidziŵa?” Akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Iye ankateteza anthu osauka ndi osowa, ndipo zonse zinkamuyendera bwino. Kodi zimenezi sindiye tanthauzo la kudziwa Ine?” akutero Yehova. Onani mutuwo |