Yeremiya 22:14 - Buku Lopatulika14 amene ati, Ndidzadzimangira ndekha nyumba yotakata ndi zipinda zapamwamba zazikulu, nadziboolera mazenera; navundikira tsindwi lam'kati ndi mikungudza, naipaka ndi utoto wofiira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 amene ati, Ndidzadzimangira ndekha nyumba yotakata ndi zipinda zapamwamba zazikulu, nadziboolera mazenera; navundikira chindwi lam'kati ndi mikungudza, naipaka ndi utoto wofiira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Munthuyo amanena kuti, ‘Ndidzadzimangira nyumba yaikulu, ya zipinda zam'mwamba zikuluzikulu, ndidzaikamo mawindo, ndi kukhomamo matabwa a mkungudza, ndipo ndidzaipaka utoto wofiira.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Munthuyo amati, ‘Ndidzadzimangira nyumba yayikulu ya zipinda zikuluzikulu zamʼmwamba.’ Kotero ndidzapanga mazenera akuluakulu, ndi kukhomamo matabwa a mkungudza ndi kukongoletsa ndi makaka ofiira. Onani mutuwo |