Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 22:12 - Buku Lopatulika

12 koma kumene anamtengera iye ndende, kumeneko adzafa, ndipo sadzaonanso dziko ili.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 koma kumene anamtengera iye ndende, kumeneko adzafa, ndipo sadzaonanso dziko ili.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Adzafera ku dziko laukapolo, ndipo sadzaliwonanso dziko lino.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iyeyo adzafera ku ukapoloko. Sadzalionanso dziko lino.”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 22:12
6 Mawu Ofanana  

Masiku ake Farao Neko mfumu ya Aejipito anakwerera mfumu ya Asiriya ku mtsinje wa Yufurate; ndipo mfumu Yosiya anatuluka kuponyana naye, koma anapha Yosiya ku Megido, atamuona.


Ndipo Farao Neko analonga ufumu Eliyakimu mwana wa Yosiya, m'malo mwa Yosiya atate wake, nasanduliza dzina lake likhale Yehoyakimu; koma anapita naye Yehowahazi, nafika iye mu Ejipito, nafa komweko.


Chifukwa chake Yehova atero za Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda: Sadzamlira iye, kuti, Kalanga ine mbale wanga! Kapena, Kalanga ine mlongo wanga! Sadzamlira, kuti, Kalanga ine mbuye! Kapena, Kalanga ine ulemerero wake!


Koma kudziko kumene moyo wao ukhumba kubwerera, kumeneko sadzabwerako.


Pakuti atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Monga mkwiyo wanga ndi ukali wanga wathiridwa kwa okhala mu Yerusalemu, momwemo ukali wanga udzathiridwa pa inu, pamene mudzalowa mu Ejipito; ndipo mudzakhala chitukwano, ndi chizizwitso, ndi chitemberero, ndi chitonzo; ndipo simudzaonananso malo ano.


Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa