Yeremiya 22:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti Yehova atero za Salumu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, amene analamulira m'malo mwake mwa Yosiya atate wake, amene anatuluka m'malo muno: Sadzabweranso kuno nthawi iliyonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti Yehova atero za Salumu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, amene analamulira m'malo mwake mwa Yosiya atate wake, amene anatuluka m'malo muno: Sadzabweranso kuno nthawi iliyonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Paja Salumu, mwana wa Yosiya, mfumu ya ku Yuda, adaloŵa m'malo mwa atate ake pa mpando waufumu umene adausiya. Tsono ponena za amene uja Chauta akuti, “Iyeyo sadzabwereranso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Pakuti zimene Yehova akunena za Yehowahazi mwana wa Yosiya, amene anatenga mpando waufumu wa Yuda mʼmalo mwa abambo ake koma nʼkuwusiya ndi izi: “Iye sadzabwereranso. Onani mutuwo |