Yeremiya 21:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo uziti kwa anthu awa, Yehova atero, Taonani, ndaika pamaso panu njira ya moyo ndi njira ya imfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo uziti kwa anthu awa, Yehova atero, Taonani, ndaika pamaso panu njira ya moyo ndi njira ya imfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta akunena kuti, “Anthu ameneŵa udzaŵauzenso kuti asankhulepo: kodi afuna moyo kapena imfa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Yehova anati ndiwawuzenso anthu amenewa kuti asankhe pakati pa moyo ndi imfa. Onani mutuwo |