Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 21:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo uziti kwa anthu awa, Yehova atero, Taonani, ndaika pamaso panu njira ya moyo ndi njira ya imfa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo uziti kwa anthu awa, Yehova atero, Taonani, ndaika pamaso panu njira ya moyo ndi njira ya imfa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Chauta akunena kuti, “Anthu ameneŵa udzaŵauzenso kuti asankhulepo: kodi afuna moyo kapena imfa?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 “Yehova anati ndiwawuzenso anthu amenewa kuti asankhe pakati pa moyo ndi imfa.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 21:8
6 Mawu Ofanana  

M'khwalala la chilungamo muli moyo; m'njira ya mayendedwe ake mulibe imfa.


Ndipo Yeremiya anati kwa Zedekiya, Atero Yehova, Mulungu wa makamu, Mulungu wa Israele: Ngati mudzatulukira kwa akulu a mfumu ya ku Babiloni, mudzakhala ndi moyo, ndipo mzindawu sudzatenthedwa ndi moto; ndipo mudzakhala ndi moyo ndi banja lanu;


Taonani, ndilikuika pamaso panu lero dalitso ndi temberero;


Tapenyani, ndaika pamaso panu lero lino moyo ndi zokoma, imfa ndi zoipa;


Ndichititsa mboni lero, kumwamba ndi dziko lapansi zitsutse inu; ndaika pamaso panu moyo ndi imfa, mdalitso ndi temberero; potero, sankhani moyo, kuti mukhale ndi moyo, inu ndi mbeu zanu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa