Yeremiya 21:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Ine mwini ndidzamenyana ndi inu ndi dzanja lotambasuka ndi mkono wamphamvu, m'mkwiyo, ndi m'kupsa mtima, ndi mu ukali waukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Ine mwini ndidzamenyana ndi inu ndi dzanja lotambasuka ndi mkono wamphamvu, m'mkwiyo, ndi m'kupsa mtima, ndi m'ukali waukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ineyo mwiniwakene ndi mkono wanga wamphamvu, ndidzamenyana nanu nkhondo inuyo, ndili wopsa mtima, wokalipa ndi wokwiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ineyo mwini wakene ndi mkono wotambasula ndi dzanja lamphamvu, ndidzachita nanu nkhondo ndili wokwiya, wokalipa ndi waukali. Onani mutuwo |