Yeremiya 21:13 - Buku Lopatulika13 Taonani, Ine ndine mdani wako, iwe wokhala m'chigwa, ndi pa thanthwe la m'chidikha, ati Yehova; inu amene muti, Ndani adzatsikira kumenyana ndi ife? Ndani adzalowa m'zokhalamo zathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Taonani, Ine ndine mdani wako, iwe wokhala m'chigwa, ndi pa thanthwe la m'chidikha, ati Yehova; inu amene muti, Ndani adzatsikira kumenyana ndi ife? Ndani adzalowa m'zokhalamo zathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “ ‘Ndikukuimbani mlandu, inu anthu okhala m'chigwa inu okhala ngati thanthwe lapachidikha,’ ” akutero Chauta. “Inu amene mumati, ‘Ndani angatithire nkhondo? Ndani angathe kuloŵa m'malinga mwathu?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndidzalimbana nanu, inu amene mukukhala pamwamba pa chigwa, inu okhala ngati thanthwe lapachidikha, akutero Yehova. Inu amene mumanena kuti, ‘Ndani amene angabwere kudzalimbana nafe? Ndani amene angathe kulowa mʼmalinga mwathu?’ Onani mutuwo |