Yeremiya 21:12 - Buku Lopatulika12 Nyumba ya Davide iwe, Yehova atero, Chita chiweruzo m'mawa, ndi kumlanditsa amene afunkhidwa m'dzanja la wosautsa, kungatuluke kupsa mtima kwanga ngati moto, ndi kutentha kosazimika, chifukwa cha ntchito zanu zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Nyumba ya Davide iwe, Yehova atero, Chita chiweruzo m'mawa, ndi kumlanditsa amene afunkhidwa m'dzanja la wosautsa, kungatuluke kupsa mtima kwanga ngati moto, ndi kutentha kosazimika, chifukwa cha ntchito zanu zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu a m'banja la Davide, Chauta akunena kuti: “ ‘Muziweruza motsata chilungamo m'maŵa mulimonse, ndipo muzipulumutsa kwa anthu ozunza, aliyense amene katundu wake wabedwa, kuwopa kuti mkwiyo wanga ungayake nkukhala wosazimika, chifukwa cha machimo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 inu a mʼbanja la Davide, Yehova akuti, “ ‘Weruzani mwachilungamo mmawa uliwonse; pulumutsani mʼdzanja la wozunza aliyense amene walandidwa katundu wake, kuopa kuti ukali wanga ungabuke ndi kuyaka ngati moto wosazimitsika chifukwa cha zoyipa zimene mwachita. Onani mutuwo |