Yeremiya 21:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo za nyumba ya mfumu ya Yuda, tamvani mau a Yehova: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo za nyumba ya mfumu ya Yuda, tamvani mau a Yehova: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Tsono banja laufumu la ku Yuda uliwuze kuti, ‘Imvani mau a Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Komanso, uwuze banja laufumu la Yuda kuti, ‘Imva mawu a Yehova; Onani mutuwo |