Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 21:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo za nyumba ya mfumu ya Yuda, tamvani mau a Yehova:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo za nyumba ya mfumu ya Yuda, tamvani mau a Yehova:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 “Tsono banja laufumu la ku Yuda uliwuze kuti, ‘Imvani mau a Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 “Komanso, uwuze banja laufumu la Yuda kuti, ‘Imva mawu a Yehova;

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 21:11
6 Mawu Ofanana  

Nenani kwa mfumu ndi kwa amake wa mfumu, Dzichepetseni, khalani pansi; pakuti zapamtu zanu zagwa, korona wanu wokoma.


ndipo uziti kwa iwo, Tamvani mau a Yehova, inu mafumu a Yuda, ndi Ayuda onse, ndi onse okhala mu Yerusalemu, amene alowa pa zipatazi;


Nyumba ya Davide iwe, Yehova atero, Chita chiweruzo m'mawa, ndi kumlanditsa amene afunkhidwa m'dzanja la wosautsa, kungatuluke kupsa mtima kwanga ngati moto, ndi kutentha kosazimika, chifukwa cha ntchito zanu zoipa.


Yehova atero: Tsikira kunyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa,


Chifukwa chake Yehova atero za Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda: Sadzamlira iye, kuti, Kalanga ine mbale wanga! Kapena, Kalanga ine mlongo wanga! Sadzamlira, kuti, Kalanga ine mbuye! Kapena, Kalanga ine ulemerero wake!


Ndipo ndinati, Imvanitu, inu akulu a Yakobo, ndi oweruza a nyumba ya Israele; simuyenera kodi kudziwa chiweruzo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa