Yeremiya 21:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti ndaika nkhope yanga pa mzinda uwu ndiuchitire choipa, si chabwino, ati Yehova; ndipo udzapatsidwa m'dzanja la mfumu ya ku Babiloni, ndipo iye adzautentha ndi moto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti ndaika nkhope yanga pa mudzi uwu ndiuchitire choipa, si chabwino, ati Yehova; ndipo udzapatsidwa m'dzanja la mfumu ya ku Babiloni, ndipo iye adzautentha ndi moto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Mzinda umenewu ndatsimikiza kuti ndidzauchita zoipa osati zabwino ai. Udzaperekedwa kwa mfumu ya ku Babiloni ndipo iyeyo adzautentha ndi moto.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ine ndatsimikiza kuchitira mzinda uno choyipa osati chabwino, akutero Yehova. Udzaperekedwa mʼdzanja la mfumu ya ku Babuloni, ndipo iyeyo adzawutentha ndi moto. Onani mutuwo |