Yeremiya 21:1 - Buku Lopatulika1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, pamene Zedekiya mfumu anatuma kwa iye Pasuri mwana wa Malikiya, ndi Zefaniya mwana wake wa Maaseiya wansembe, akati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, pamene Zedekiya mfumu anatuma kwa iye Pasuri mwana wa Malikiya, ndi Zefaniya mwana wake wa Maaseiya wansembe, akati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Zedekiya, mfumu ya ku Yuda, adatuma Pasuri mwana wa Malakiya, ndiponso wansembe Zefaniya mwana wa Maseiya, naŵauza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mfumu Zedekiya inatuma Pasuri mwana wa Malikiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa Yeremiya. Onani mutuwo |