Yeremiya 20:7 - Buku Lopatulika7 Yehova, mwandikopa ine, ndipo ndinakopedwa; muli ndi mphamvu koposa ine, ndipo mwapambana; ine ndikhala choseketsa dzuwa lonse, onse andiseka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Yehova, mwandikopa ine, ndipo ndinakopedwa; muli ndi mphamvu koposa ine, ndipo mwalakika; ine ndikhala choseketsa dzuwa lonse, onse andiseka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu Chauta, mwandipusitsa ine, ndipo ndapusadi. Inu ndinu amphamvu kuposa ine, ndipo mwandipambana. Aliyense akundiseka tsiku lonse, aliyense akundinyodola kosalekeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu Yehova, mwandinamiza, ndipo ndinapusadi; Inu ndi wamphamvu kuposa ine ndipo munandipambana. Anthu akundinyoza tsiku lonse. Aliyense akundiseka kosalekeza. Onani mutuwo |