Yeremiya 20:18 - Buku Lopatulika18 Chifukwa chanji ndinatuluka m'mimba kuti ndione kutopa ndi kulira, kuti masiku anga athe ndi manyazi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Chifukwa chanji ndinatuluka m'mimba kuti ndione kutopa ndi kulira, kuti masiku anga athe ndi manyazi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Kodi chifukwa chiyani ndidabadwa? Kodi ndidabadwira mavuto ndi chisoni, kuti moyo wanga ukhale wa manyazi okhaokha? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Kodi ndinabadwira mavuto ndi chisoni kuti moyo wanga ukhale wamanyazi wokhawokha? Onani mutuwo |