Yeremiya 20:17 - Buku Lopatulika17 chifukwa sanandiphe ine m'mimba; kuti mai wanga akhale manda anga, ndi mimba yake yaikulu nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 chifukwa sanandiphe ine m'mimba; kuti mai wanga akhale manda anga, ndi mimba yake yaikulu nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 chifukwa choti sadandiphere m'mimba, kuti mai wanga asanduke manda anga, ndipo kuti mimba yake ikhale chitupire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Chifukwa sanandiphere mʼmimba, kuti amayi anga asanduke manda anga, mimba yawo ikhale yayikulu mpaka kalekale. Onani mutuwo |