Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 20:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Pasuri mwana wake wa Imeri wansembe, amene anali kapitao wamkulu m'nyumba ya Yehova, anamva Yeremiya alikunenera zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Pasuri mwana wake wa Imeri wansembe, amene anali kapitao wamkulu m'nyumba ya Yehova, anamva Yeremiya alikunenera zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Wansembe Pasuri, mwana wa Imeri, amene anali kapitao wamkulu ku Nyumba ya Chauta, adamva Yeremiya akulosa zinthu zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Wansembe Pasuri mwana wa Imeri, woyangʼanira wamkulu wa Nyumba ya Yehova, anamva Yeremiya akulosera zinthu zimenezi.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 20:1
11 Mawu Ofanana  

Ndipo mkulu wa olindirira anatenga Seraya wansembe wamkulu, ndi Zefaniya wansembe wachiwiri, ndi olindira pakhomo atatu;


wakhumi ndi chisanu Biliga, wakhumi ndi chisanu ndi chimodzi Imeri,


ndi Azariya mwana wa Hilikiya, mwana wa Mesulamu, mwana wa Zadoki, mwana wa Meraiyoti, mwana wa Ahitubi, mtsogoleri wa m'nyumba ya Mulungu;


Ndi akulu ake anapatsa nsembe yaufulu kwa anthu, kwa ansembe, ndi kwa Alevi. Hilikiya ndi Zekariya ndi Yehiyele, atsogoleri a m'nyumba ya Mulungu, anapatsa ansembe zoweta zazing'ono zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi, ndi ng'ombe mazana atatu, zikhale nsembe za Paska.


Ndipo iwe, Pasuri, ndi onse okhala m'nyumba mwako mudzanka kundende; ndipo udzafika ku Babiloni, ndi pamenepo udzafa, ndi pamenepo udzaikidwa, iwe, ndi mabwenzi ako onse, amene unawanenera mabodza.


Yehova anakuyesa iwe wansembe m'malo mwa Yehoyada wansembe, kuti iwe ndi anzako mudzakhale akapitao m'nyumba ya Yehova, oyang'anira munthu yense wamisala, wodziyesa mneneri, kuti umuike iye m'zigologolo ndi m'goli.


Ndipo akulu anakwiyira Yeremiya, nampanda iye, namuika m'nyumba yandende m'nyumba ya Yonatani mlembi; pakuti anaiyesa ndende.


Koma m'mene analikulankhula ndi anthu, ansembe ndi mdindo wa ku Kachisi ndi Asaduki anadzako,


Koma m'mene anamva mau awa mdindo wa Kachisi ndi ansembe aakulu anathedwa nzeru ndi iwo aja, kuti ichi chidzatani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa