Yeremiya 2:37 - Buku Lopatulika37 Koma udzatuluka kwa iyenso, manja ako pamutu pako; pakuti Yehova wakana zokhulupirira zako, ndipo sudzapindula m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Koma udzatuluka kwa iyenso, manja ako pamtu pako; pakuti Yehova wakana zokhulupirira zako, ndipo sudzapindula m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Mudzatuluka kumeneko aliyense atagwirira manja ku mutu. Ine Chauta ndidaŵakana amene inu mumagonerapo, ndipo anthuwo sadzakuthandizani mpang'ono pomwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Mudzachokanso kumeneko manja ali kunkhongo. Popeza Ine Yehova ndawakana anthu amene munkawadalira, choncho sadzakuthandizani konse. Onani mutuwo |