Yeremiya 2:36 - Buku Lopatulika36 Bwanji uyendayenda kwambiri ndi kusintha njira yako? Udzachitanso manyazi ndi Ejipito monga unachita manyazi ndi Asiriya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Bwanji uyendayenda kwambiri ndi kusintha njira yako? Udzachitanso manyazi ndi Ejipito monga unachita manyazi ndi Asiriya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Bwanji mukudzipeputsa nokha posinthasintha njira zanu! Ejipito adzakugwiritsani mwala monga muja adakuchititsirani manyazi Aasiriya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Chifukwa chiyani mukunkabe nimusinthasintha njira zanu? Aigupto adzakukhumudwitsani monga momwe Asiriya anakuchititsani manyazi. Onani mutuwo |