Yeremiya 2:32 - Buku Lopatulika32 Kodi angathe namwali kuiwala zokometsera zake, kapena mkwatibwi zovala zake? Koma anthu anga andiiwala Ine masiku osawerengeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Kodi angathe namwali kuiwala zokometsera zake, kapena mkwitibwi zovala zake? Koma anthu anga andiiwala Ine masiku osawerengeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Kodi namwali amaiŵala zokongoletsera zake, kapena mkwati kuiŵala zovala zake zaukwati? Komabe anthu anga andiiŵala Ine masiku osaŵerengeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Kodi namwali amayiwala zokongoletsera zake, kapena kuyiwala zovala zake za ukwati? Komatu anthu anga andiyiwala masiku osawerengeka. Onani mutuwo |