Yeremiya 2:31 - Buku Lopatulika31 Mbadwo inu, taonani mau a Yehova. Kodi ndakhala kwa Israele chipululu? Kapena dziko la mdima woti bii? Chifukwa ninji ati anthu anga, Tamasuka sitidzabweranso konse kwa Inu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Mbadwo inu, taonani mau a Yehova. Kodi ndakhala kwa Israele chipululu? Kapena dziko la mdima woti bii? Chifukwa ninji ati anthu anga, Tamasuka sitidzabweranso konse kwa Inu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Inu anthu amakono, imvani mau a Chauta. “Kodi ndakhala ngati chipululu kwa Israele, kapena ngati dziko la mdima wandiweyani? Chifukwa chiyani tsono anthu anga akunena kuti, ‘Ndife mfulu, sitidzabweranso kwa Inu?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 “Inu anthu a mʼbado uno, ganizirani bwino mawu a Yehova: “Kodi Ine ndinakhalapo ngati chipululu kwa Israeli kapena ngati dziko la mdima wandiweyani? Chifukwa chiyani anthu anga akunena kuti, ‘Ife tili ndi ufulu omayendayenda; sitidzabweranso kwa Inu’? Onani mutuwo |