Yeremiya 2:30 - Buku Lopatulika30 Ndapanda ana anu mwachabe; sanamvere kulanga; lupanga lanu ladya aneneri anu, monga mkango wakuononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndapanda ana anu mwachabe; sanamvere kulanga; lupanga lanu ladya aneneri anu, monga mkango wakuononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Ndidalanga ana anu popanda phindu, sadaphunzirepo nkanthu komwe. Monga mkango wolusa mudapha aneneri anu ndi lupanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Ine ndinalanga anthu ako popanda phindu; iwo sanaphunzirepo kanthu. Monga mkango wolusa, lupanga lanu lapha aneneri anu. Onani mutuwo |