Yeremiya 2:28 - Buku Lopatulika28 Koma ili kuti milungu yako imene wadzipangira? Iuke, ikupulumutse iwe m'nthawi ya kuvutidwa kwako; pakuti milungu yako ilingana ndi kuchuluka kwa mizinda yako, Yuda iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Koma ili kuti milungu yako imene wadzipangira? Iuke, ikupulumutse iwe m'nthawi ya kuvutidwa kwako; pakuti milungu yako ilingana ndi kuchuluka kwa midzi yako, Yuda iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Nanga milungu yanu ili kuti, milungu ija mudadzipangira ija? Idzambatuketu, ngati ingathe kukupulumutsani pa nthaŵi yanu ya mavuto. Inu anthu a ku Yuda, milungu yanu ndi yambiri, kuchuluka kwake monga momwe iliri mizinda yanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Nanga ili kuti milungu yanu imene munadzipangira nokha? Ibweretu ngati ingathe kukupulumutsani pamene muli pamavuto! Inu anthu a ku Yuda, milungu yanu ndi yambiri kuchuluka kwake ngati mizinda yanu. Onani mutuwo |