Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 2:24 - Buku Lopatulika

24 mbidzi yozolowera m'chipululu, yopumira mphepo pakufuna pake; pokomana nayo ndani adzaibweza? Onse amene aifuna sadzadzilemetsa; adzaipeza m'mwezi wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 mbidzi yozolowera m'chipululu, yopumira mphepo pakufuna pake; pokomana nayo ndani adzaibweza? Onse amene aifuna sadzadzilemetsa; adzaipeza m'mwezi wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Wakhala ngati mbidzi yaikazi yozoloŵera m'chipululu, yonka nipunika pa nthaŵi yake yachisika. Kodi angailetse chilakolako chakecho ndani? Mphongo iliyonse yoikhumba sidzavutika, idzaipeza pa nthaŵi yakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 wakhala ngati mbidzi yozolowera mʼchipululu, yonka ninunkhiza pa nthawi yachisika. Ndani angayiretse chilakolako chakecho? Mphongo iliyonse yoyikhumba sidzavutika. Pa nthawi yachisika chakecho mphongoyo idzayipeza.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 2:24
8 Mawu Ofanana  

Koma munthu wopanda pake asowa nzeru, ngakhale munthu abadwa ngati mwanawabulu.


Ukhoza kodi kuwerenga miyezi yakuzipitira, kapena udziwa nyengo yoti ziswane?


Mbidzi zinaima pamapiri oti see, zipumira mphepo wefuwefu ngati ankhandwe; maso ao alema, chifukwa palibe udzu.


amene ati kwa mtengo, Iwe ndiwe atate wanga; ndi kwa mwala, Wandibala; pakuti anandipatsa Ine mbuyo, si nkhope yao; koma m'nthawi ya kuvutidwa kwao adzati, Ukani, tipulumutseni.


Anthu amaninkha akazi onse achigololo mphatso, koma iwe umaninkha mabwenzi ako onse mphatso zako ndi kuwalipira, kuti akudzere kuchokera kumbali zonse, kuti achite nawe chigololo.


Ndidzamuka ndi kubwerera kunka kumalo kwanga, mpaka adzavomereza kupalamula kwao, nafunafuna nkhope yanga; m'msauko mwao adzandifunafuna mwachangu.


Pakuti anakwera kunka ku Asiriya, ngati mbidzi ya pa yokha mwini wake; Efuremu walembera omkonda ngati antchito.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa