Yeremiya 2:23 - Buku Lopatulika23 Bwanji uti, Sindinaipitsidwe, sindinatsate Abaala? Ona njira yako m'chigwa, dziwa chimene wachichita; ndiwe ngamira yothamanga yoyenda m'njira zake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Bwanji uti, Sindinaipitsidwa, sindinatsata Abaala? Ona njira yako m'chigwa, dziwa chimene wachichita; ndiwe ngamira yothamanga yoyenda m'njira zake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 “Uneneranji kuti, ‘Ine sindidadziipitse, sindidatsate Baala?’ Kumbukira m'mene udachimwira m'chigwamo, zindikira zimene wachita. Wakhala ngati ngamira yaikazi, yothamanga uku ndi uku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 “Iwe ukunena bwanji kuti, ‘Ine sindinadziyipitse; sindinatsatire Abaala’? Takumbukira mmene unkandichimwira mʼchigwa muja; zindikira bwino zomwe wachita. Iwe uli ngati ngamira yayikazi yaliwiro yomangothamanga uku ndi uku, Onani mutuwo |