Yeremiya 2:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti ngakhale usamba ndi soda, ndi kudzitengera sopo wambiri, mphulupulu zako zidziwika pamaso panga, ati Yehova Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti ngakhale usamba ndi soda, ndi kudzitengera sopo wambiri, mphulupulu zako zidziwika pamaso panga, ati Yehova Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ngakhale usambire soda, ngakhale usambire sopo wambiri, kuthimbirira kwa tchimo lako kumaonekabe pamaso panga,” akuterotu Ambuye Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ngakhale utasamba ndi soda kapena kusambira sopo wambiri, kuthimbirira kwa machimo ako kumaonekabe pamaso panga,” akutero Ambuye Yehova. Onani mutuwo |