Yeremiya 2:14 - Buku Lopatulika14 Kodi Israele ndi mtumiki? Kodi ndiye kapolo wobadwa m'nyumba? Afunkhidwa bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Kodi Israele ndi mtumiki? Kodi ndiye kapolo wobadwa m'nyumba? Afunkhidwa bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Israele si kapolotu ai, sadabadwire mu ukapolo. Nanga chifukwa chiyani amuwononga chotere? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Israeli si wantchito kapena kapolo wobadwira mʼnyumba, ayi. Nanga nʼchifukwa chiyani amuwononga chotere? Onani mutuwo |