Yeremiya 19:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ndidzadyetsa iwo mnofu wa ana ao aamuna ndi aakazi, ndipo adzadya yense mnofu wa mbale wake, m'nkhondo yozinga ndi m'kupsinjikako, kumene adani ao, ndi iwo akufuna moyo wao, adzapsinja iwo nako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ndidzadyetsa iwo mnofu wa ana ao aamuna ndi aakazi, ndipo adzadya yense mnofu wa mbale wake, m'nkhondo yozinga ndi m'kupsinjikako, kumene adani ao, ndi iwo akufuna moyo wao, adzapsinja iwo nako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndidzaumiriza anthuwo kuti adye ana ao omwe aamuna ndi aakazi. Adzadyana choncho pa nthaŵi yoopsa pamene adzazingidwa ndi adani ao ofuna kuŵazunza.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Adani awo adzawuzinga mzindawo kufuna kuwapha motero kuti anthu a mʼkatimo adzafika pomadyana wina ndi mnzake. Adzadya ana awo aamuna ndi ana awo aakazi.’ Onani mutuwo |