Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 19:12 - Buku Lopatulika

12 Ndidzatero ndi malo ano, ati Yehova, ndi okhalamo, kusanduliza mzinda uwu ngati Tofeti;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndidzatero ndi malo ano, ati Yehova, ndi okhalamo, kusanduliza mudzi uwu ngati Tofeti;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Umu ndimo m'mene ndidzaŵachitire malo ano pamodzi ndi anthu ake omwe. Mzindawu ndidzausandutsa ngati Tofeti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Umu ndi mmene ndidzachitire ndi malo ano pamodzi ndi anthu okhalamo, akutero Yehova. Ndidzasandutsa mzindawu kukhala ngati Tofeti.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 19:12
4 Mawu Ofanana  

polankhula Iye, pali unyinji wa madzi m'mwamba, ndipo akweretsa nkhungu ku malekezero a dziko lapansi, alenga mphezi idzetse mvula, natulutsa mphepo m'zosungira zake.


kuti ndikalimbikitse lumbiro limene ndinalumbirira makolo anu, ndiwapatse dziko moyenda mkaka ndi uchi, monga lero lomwe. Ndipo ndinayankha, ndi kuti, Amen, Yehova.


nuziti kwa iwo, Yehova wa makamu atero: Chomwecho ndidzaphwanya anthu awa ndi mzinda uwu, monga aphwanya mbiya ya woumba, imene sangathe kuiumbanso, ndipo adzaika maliro mu Tofeti, mpaka mulibe malo akuikamo.


ndi nyumba za Yerusalemu, ndi nyumba za mafumu a Yuda, zimene ziipitsidwa, zidzanga malo a Tofeti, ndizo nyumba zonse anafukizira khamu lonse la kumwamba pa matsindwi ao, ndi kuithirira milungu ina nsembe zothira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa