Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 19:10 - Buku Lopatulika

10 Pamenepo uziphwanya nsupa pamaso pa anthu otsagana ndi iwe,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Pamenepo uziphwanya nsupa pamaso pa anthu otsagana ndi iwe,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 “Tsono iweyo udzaphwanye mtsuko uja, anthu amene udzapite nawowo akuwona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 “Tsono iwe udzaphwanye mtsukowo anthu amene udzapite nawowo akuona,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 19:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye adzagumulapo, monga mbiya ya woumba isweka, ndi kuiswaiswa osaileka; ndipo sipadzapezedwa m'zigamphu zake phale lopalira moto pachoso, ngakhale lotungira madzi padziwe.


Atero Yehova, Pita, nugule nsupa ya woumba, nutenge akulu a anthu, ndi akulu a ansembe;


Chifukwa chake, taonani, masiku adza, ati Yehova, amene ndidzatuma kwa iye otsanula, amene adzamtsanula iye; adzataya za mbiya zake, nadzaswa zipanda zao.


Pamwamba pa matsindwi a Mowabu ndi m'miseu mwake muli kulira monsemonse; pakuti ndaswa Mowabu monga mbiya m'mene mulibe chikondwero, ati Yehova.


anadza kwa Iye mkazi, anali nayo nsupa ya alabastero ndi mafuta onunkhira bwino a mtengo wapatali, nawatsanulira pamutu pake, m'mene Iye analikukhala pachakudya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa