Yeremiya 19:1 - Buku Lopatulika1 Atero Yehova, Pita, nugule nsupa ya woumba, nutenge akulu a anthu, ndi akulu a ansembe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Atero Yehova, Pita, nugule nsupa ya woumba, nutenge akulu a anthu, ndi akulu a ansembe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta adandiwuza kuti, “Pita ukagule mtsuko wadothi kwa munthu woumba. Utenge akuluakulu ena, ndiponso ansembe ena okhwimapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anandiwuza kuti, “Pita ukagule mʼphika wadothi kwa munthu wowumba. Utenge akuluakulu ena a anthuwa ndi ansembe Onani mutuwo |