Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 18:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Tsono Chauta adafunsa kuti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Kenaka Yehova anandiwuza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 18:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene mbiya alikuiumba ndi dothi inaonongeka m'dzanja la woumba, anaiumbanso mbiya ina, monga kunamkomera woumba kuiumba.


Nyumba ya Israele inu, kodi sindingathe kuchita ndi inu monga woumba uyu? Ati Yehova. Taonani, monga dothi m'dzanja la woumba, momwemo inu m'dzanja langa, nyumba ya Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa