Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 18:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo ndinatsikira kunyumba ya woumba, ndipo, taonani, anaumba ntchito yake ndi njinga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo ndinatsikira kunyumba ya woumba, ndipo, taonani, anaumba ntchito yake ndi njinga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Motero ndidatsikira ku nyumba ya woumba mbiya, ndipo ndidampeza akuumba mbiya pa mkombero.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Choncho ndinatsikira ku nyumba ya wowumba mbiya, ndipo ndinamuona akuwumba mbiya pa mkombero.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 18:3
5 Mawu Ofanana  

Tauka, tatsikira kunyumba ya woumba, pamenepo ndidzakumvetsa mau anga.


Ndipo pamene mbiya alikuiumba ndi dothi inaonongeka m'dzanja la woumba, anaiumbanso mbiya ina, monga kunamkomera woumba kuiumba.


Koma Yona ananyamuka kuti athawire ku Tarisisi, kuzemba Yehova; ndipo anatsikira ku Yopa, napezako chombo chomuka ku Tarisisi, napereka ndalama zake, natsikira m'menemo, kuti apite nao ku Tarisisi kuzemba Yehova.


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


Potero, Mfumu Agripa, sindinakhale ine wosamvera masomphenya a Kumwamba;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa